14 Ineyo sindidzadzitama pa chifukwa china chilichonse, koma chifukwa cha mtengo wozunzikirapo+ wa Ambuye wathu Yesu Khristu basi. Kudzera mwa ameneyu, kwa ine dziko lapansi lapachikidwa, ndipo malinga ndi kuona kwa dziko lapansi,+ ineyo ndapachikidwa.