Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 16:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Kenako Yesu anauza ophunzira ake kuti: “Ngati munthu akufuna kunditsatira, adzikane yekha ndi kunyamula mtengo wake wozunzikirapo* ndipo anditsatire mosalekeza.+

  • Maliko 8:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Kenako iye anaitana khamu la anthu pamodzi ndi ophunzira ake ndi kuwauza kuti: “Ngati munthu akufuna kunditsatira, adzikane yekha ndi kunyamula mtengo wake wozunzikirapo,* ndi kunditsatira mosalekeza.+

  • Luka 9:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Kenako anauza onse kuti: “Ngati munthu akufuna kunditsatira, adzikane yekha+ ndi kunyamula mtengo wake wozunzikirapo* tsiku ndi tsiku ndi kunditsatira mosalekeza.+

  • Agalatiya 6:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ineyo sindidzadzitama pa chifukwa china chilichonse, koma chifukwa cha mtengo wozunzikirapo+ wa Ambuye wathu Yesu Khristu basi. Kudzera mwa ameneyu, kwa ine dziko lapansi lapachikidwa, ndipo malinga ndi kuona kwa dziko lapansi,+ ineyo ndapachikidwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena