20 Tsoka kwa amene akunena kuti chabwino n’choipa ndipo choipa n’chabwino,+ amene akuika mdima m’malo mwa kuwala ndi kuwala m’malo mwa mdima, amene akuika zowawa m’malo mwa zotsekemera,* ndi zotsekemera m’malo mwa zowawa.+
48 Aliyense wondinyalanyaza ndi kusalandira mawu anga, ali naye mmodzi womuweruza. Mawu+ amene ine ndalankhula ndi amene adzamuweruze pa tsiku lomaliza.