Mateyu 8:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Kenako panyanjapo panabuka mphepo yamphamvu moti mafunde anali kulowa m’ngalawamo, koma iye anali m’tulo.+ Mateyu 14:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Pa nthawiyi n’kuti ngalawa ija itapita kutali pakati pa madzi, ndipo inali kukankhidwa mwamphamvu ndi mafunde+ chifukwa anali kulimbana ndi mphepo yamphamvu. Maliko 6:48 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 48 Kenako anaona ophunzirawo akupalasa movutika,+ chifukwa anali kulimbana ndi mphepo yamphamvu. Uwu unali m’bandakucha pafupifupi pa ulonda wachinayi,* ndipo iye anawalondola akuyenda panyanja. Koma ophunzirawo anaona ngati akufuna kuwapitirira.
24 Kenako panyanjapo panabuka mphepo yamphamvu moti mafunde anali kulowa m’ngalawamo, koma iye anali m’tulo.+
24 Pa nthawiyi n’kuti ngalawa ija itapita kutali pakati pa madzi, ndipo inali kukankhidwa mwamphamvu ndi mafunde+ chifukwa anali kulimbana ndi mphepo yamphamvu.
48 Kenako anaona ophunzirawo akupalasa movutika,+ chifukwa anali kulimbana ndi mphepo yamphamvu. Uwu unali m’bandakucha pafupifupi pa ulonda wachinayi,* ndipo iye anawalondola akuyenda panyanja. Koma ophunzirawo anaona ngati akufuna kuwapitirira.