Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 11:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atate wanga wapereka zinthu zonse kwa ine, ndipo palibe amene akum’dziwa bwino Mwana koma Atate+ okha, komanso palibe amene akuwadziwa bwino Atate koma Mwana yekha+ ndi aliyense amene Mwanayo wafuna kumuululira za Atatewo.+

  • Yohane 3:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Atate amakonda Mwana wake+ ndipo anapereka zinthu zonse m’manja mwake.+

  • Yohane 17:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Zonse zimene ndili nazo ndi zanu ndipo zanu zonse ndi zanga.+ Ine ndalemekezeka pakati pawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena