Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 41:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Iweyo ukhala woyang’anira nyumba yanga,+ ndipo anthu anga onse azimvera iweyo.+ Ine ndikhala wokuposa pa ufumu wokha.”+

  • Genesis 41:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Farao anauzanso Yosefe kuti: “Tsopano ndikukuika kukhala woyang’anira dziko lonse la Iguputo.”+

  • Genesis 41:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Yosefe anali ndi zaka 30+ pamene anayamba kutumikira Farao, mfumu ya Iguputo.

      Kenako anachoka pamaso pa Farao n’kuyamba kuyendera dziko lonse la Iguputo.

  • Salimo 105:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Anamuika kukhala mkulu woyang’anira banja lake,+

      Komanso wolamulira chuma chake chonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena