Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Luka 2:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndiyeno abusa aja anabwerera, akulemekeza ndi kutamanda Mulungu chifukwa cha zonse zimene anamva ndi kuziona, ndendende mmene anawauzira muja.

  • Machitidwe 13:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Pamene anthu a mitundu inawo anamva zimenezi, anakondwera ndi kutamanda mawu a Yehova.+ Ndipo onse amene anali ndi maganizo abwino amene akanawathandiza kukapeza moyo wosatha anakhala okhulupirira.+

  • Machitidwe 14:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Atafika kumeneko ndi kusonkhanitsa pamodzi mpingo, anafotokoza+ zinthu zambiri zimene Mulungu anachita kudzera mwa iwo. Anafotokozanso kuti Mulungu anatsegulira anthu a mitundu ina khomo lolowera m’chikhulupiriro chimenechi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena