Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ili ndi pangano limene anthu inu muyenera kulisunga, la pakati pa ine ndi inu, ngakhalenso mbewu yobwera pambuyo pa inu.+ Mwamuna aliyense pakati pa inu azidulidwa.+

  • Ekisodo 12:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Ngati mlendo wokhala nanu akufuna kuchita nanu chikondwerero cha pasika kwa Yehova, mwamuna aliyense wa m’nyumba yake adulidwe.+ Akatero atha kuchita nawo chikondwererocho, ndipo ayenera kuonedwa ngati mbadwa ya dzikolo. Koma munthu wosadulidwa asadye nawo.

  • Levitiko 12:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndipo pa tsiku la 8, khungu la mwanayo lizidulidwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena