Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 8:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ndimaganiza kuti: Munthu+ ndani kuti muzimuganizira,+

      Ndipo mwana wa munthu wochokera kufumbi ndani kuti muzimusamalira?+

  • Yesaya 64:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Komatu inu Yehova, inu ndinu Atate wathu.+ Ife ndife dongo+ ndipo inu ndinu Wotiumba.+ Tonsefe ndife ntchito ya manja anu.+

  • 1 Akorinto 15:47
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Munthu woyambayo anachokera padziko lapansi ndipo anapangidwa ndi fumbi.+ Wachiwiriyo anachokera kumwamba.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena