Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Aroma 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mulungu, amene ndikumuchitira utumiki wopatulika ndi moyo wanga wonse polalikira uthenga wabwino wonena za Mwana wake, ndiye mboni yanga+ ya mmene ndimakutchulirani m’mapemphero anga nthawi zonse.+

  • Afilipi 1:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndimachita zimenezi m’pembedzero langa lililonse limene ndimapereka mosangalala chifukwa cha nonsenu.+

  • Afilipi 1:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo ine ndikupitiriza kupemphera kuti chikondi chanu chipitirire kukula,+ limodzi ndi kudziwa zinthu molondola,+ komanso kuzindikira zinthu bwino kwambiri.+

  • Akolose 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Nthawi zonse tikamakupemphererani,+ timayamika+ Mulungu, Atate wa Ambuye wathu Yesu Khristu.

  • 1 Atesalonika 1:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Nthawi zonse timayamika Mulungu tikamatchula za inu nonse m’mapemphero athu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena