Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Atesalonika 1
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

1 Atesalonika 1:1

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Mac 15:27; 2At 1:1; 1Pe 5:12
  • +Mac 16:1
  • +Yoh 17:21
  • +1Ti 1:2

1 Atesalonika 1:2

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Aef 1:16; 2At 1:11

1 Atesalonika 1:3

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Ahe 6:10
  • +1Pe 1:3

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    3/15/2007, ptsa. 6-7

    Utumiki wa Ufumu,

    2/2000, tsa. 4

1 Atesalonika 1:4

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Akl 3:12; 2At 2:13

1 Atesalonika 1:5

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 2:4
  • +Akl 4:12
  • +1Ak 9:19

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Sukulu ya Utumiki, tsa. 194

    Nsanja ya Olonda,

    3/1/2000, ptsa. 16-17

    Utumiki wa Ufumu,

    2/2000, ptsa. 3-4

1 Atesalonika 1:6

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 11:1; Afi 3:17; 2At 3:9
  • +1Pe 2:21
  • +Mac 13:52
  • +1At 2:14

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Utumiki wa Ufumu,

    2/2000, ptsa. 3-4

1 Atesalonika 1:8

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Yes 39:5; 66:5; 1Pe 1:23
  • +2At 1:4
  • +Aro 1:8; 10:18

1 Atesalonika 1:9

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +1Ak 10:14; 12:2; Aga 4:8; 1Yo 5:21
  • +Mac 14:15; 1Ti 4:10
  • +Yoh 17:3; 1Ak 8:4

1 Atesalonika 1:10

Malifalensi Opezeka Pakati pa Tsamba

  • +Tit 2:13
  • +Mac 1:11
  • +Mac 2:24
  • +1At 5:2; 2Pe 3:12; Chv 6:17

Kalozera

  • Buku Lofufuzira Nkhani

    Nsanja ya Olonda,

    8/15/2010, tsa. 13

Mabaibulo Ena

Dinani pa nambala ya vesi kuti muone mavesi a m'Baibulo lina ofanana ndi vesilo.

Malemba Ena

1 Ates. 1:1Mac 15:27; 2At 1:1; 1Pe 5:12
1 Ates. 1:1Mac 16:1
1 Ates. 1:1Yoh 17:21
1 Ates. 1:11Ti 1:2
1 Ates. 1:2Aef 1:16; 2At 1:11
1 Ates. 1:3Ahe 6:10
1 Ates. 1:31Pe 1:3
1 Ates. 1:4Akl 3:12; 2At 2:13
1 Ates. 1:51Ak 9:19
1 Ates. 1:51Ak 2:4
1 Ates. 1:5Akl 4:12
1 Ates. 1:61Ak 11:1; Afi 3:17; 2At 3:9
1 Ates. 1:61Pe 2:21
1 Ates. 1:6Mac 13:52
1 Ates. 1:61At 2:14
1 Ates. 1:8Yes 39:5; 66:5; 1Pe 1:23
1 Ates. 1:82At 1:4
1 Ates. 1:8Aro 1:8; 10:18
1 Ates. 1:91Ak 10:14; 12:2; Aga 4:8; 1Yo 5:21
1 Ates. 1:9Mac 14:15; 1Ti 4:10
1 Ates. 1:9Yoh 17:3; 1Ak 8:4
1 Ates. 1:10Tit 2:13
1 Ates. 1:10Mac 1:11
1 Ates. 1:10Mac 2:24
1 Ates. 1:101At 5:2; 2Pe 3:12; Chv 6:17
  • Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
  • Werengani mu Baibulo la Dziko Latsopano (nwt)
  • 1
  • 2
  • 3
  • 4
  • 5
  • 6
  • 7
  • 8
  • 9
  • 10
Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
1 Atesalonika 1:1-10

1 Atesalonika

1 Ine Paulo, pamene ndili limodzi ndi Silivano+ ndi Timoteyo,+ ndikulembera mpingo wa Atesalonika wogwirizana+ ndi Mulungu Atate ndi Ambuye Yesu Khristu, kuti:

Kukoma mtima kwakukulu ndi mtendere+ zikhale nanu.

2 Nthawi zonse timayamika Mulungu tikamatchula za inu nonse m’mapemphero athu.+ 3 Timatero pakuti timakumbukira nthawi zonse ntchito zanu zachikhulupiriro,+ ndi ntchito zanu zachikondi. Timateronso pokumbukira mmene munapiririra chifukwa cha chiyembekezo+ chanu mwa Ambuye wathu Yesu Khristu, pamaso pa Mulungu wathu ndi Atate. 4 Pakuti tikudziwa, inu abale okondedwa ndi Mulungu, kuti Mulunguyo ndiye anakusankhani.+ 5 Chifukwa pamene tinali kulalikira uthenga wabwino kwa inu, sitinali kungolankhula basi, koma uthengawo unakukhudzani kwambiri, komanso unabwera limodzi ndi mphamvu+ ya mzimu woyera, ndipo unachititsa kuti mukhale otsimikiza+ mtima kwambiri. Ndipo inuyo mukudziwa zimene tinakuchitirani pofuna kukuthandizani.+ 6 Choncho munatsanzira+ ifeyo komanso munatsanzira Ambuye,+ pakuti munalandira mawuwo ndi chimwemwe cha mzimu woyera+ ngakhale kuti munali m’masautso+ ambiri, 7 moti munakhala chitsanzo kwa okhulupirira onse ku Makedoniya ndi ku Akaya.

8 Ndipotu, si kuti mawu a Yehova+ ochokera kwa inu amveka ku Makedoniya ndi ku Akaya kokha ayi, koma kwina kulikonse chikhulupiriro+ chanu mwa Mulungu chafalikira,+ moti ife sitikufunika kunenapo kanthu. 9 Pakuti iwo amanena mmene ife tinafikira pakati panu koyamba. Amanenanso mmene inu munatembenukira kwa Mulungu, kusiya mafano+ anu kuti mutumikire Mulungu wamoyo+ ndi woona,+ 10 ndi kuyembekezera+ Mwana wake kuchokera kumwamba,+ amene anamuukitsa kwa akufa.+ Mwanayo ndi Yesu, amene akutipulumutsa ku mkwiyo ukubwerawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena