Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 28:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Munthu wonyada amayambitsa mikangano,+ koma wodalira Yehova adzanenepa.+

  • Agalatiya 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Pakuti ngati wina akudziona kuti ndi wofunika pamene si wotero,+ akudzinyenga.

  • 1 Timoteyo 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Asakhale wotembenuka kumene,+ kuopera kuti angakhale wotukumuka chifukwa cha kunyada,+ n’kulandira chiweruzo chofanana ndi chimene Mdyerekezi analandira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena