Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 24:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno Mose anapita kwa anthu ndi kuwafotokozera mawu onse a Yehova ndi zigamulo zake zonse.+ Pamenepo anthu onse anayankhira pamodzi kuti: “Mawu onse amene Yehova wanena tidzachita.”+

  • Yeremiya 7:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 kuchokera tsiku limene makolo anu anatuluka m’dziko la Iguputo kufikira lero.+ Ndinapitiriza kukutumizirani atumiki anga onse aneneri, tsiku ndi tsiku ndinali kudzuka m’mawa kwambiri ndi kuwatumiza.+

  • Ezekieli 33:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Koma mawu ako akadzakwaniritsidwa, pakuti adzakwaniritsidwa ndithu,+ iwo adzadziwa kuti pakati pawo panalidi mneneri.”+

  • Luka 1:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 monga mmene iye ananenera kudzera pakamwa pa aneneri ake oyera akale,+

  • Machitidwe 3:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ameneyu kumwamba kuyenera kumusunga+ mpaka nthawi za kubwezeretsa+ zinthu zonse, kumene Mulungu ananena kudzera mwa aneneri ake oyera+ akale.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena