Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 7:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 Uyu ndi amene+ anali pakati pa mpingo+ m’chipululu limodzi ndi mngelo+ amene analankhula ndi iyeyu komanso makolo athu paphiri la Sinai. Pamenepo analandira mawu opatulika+ omwe ndi amphamvu kuti awapereke kwa inu.

  • Aroma 3:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye amaposadi ena kwambiri m’njira iliyonse. Choyamba, chifukwa chakuti mawu opatulika a Mulungu+ anaikidwa m’manja mwa Ayuda.

  • 1 Petulo 4:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ngati wina akulankhula, alankhule monga mwa mawu opatulika+ a Mulungu. Ngati wina akutumikira,+ atumikire modalira mphamvu imene Mulungu amapereka,+ kuti m’zinthu zonse Mulungu alemekezeke+ kudzera mwa Yesu Khristu. Ulemerero+ ndi mphamvu, ndi zake mpaka muyaya. Ame.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena