-
Akolose 2:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndikufuna kuti mtima wa aliyense ulimbikitsidwe,+ ndiponso kuti onse akhale ogwirizana m’chikondi.+ Achite zimenezi kuti onse alandire chuma chimene chimabwera chifukwa chomvetsa bwino zinthu,+ popanda kukayikira chilichonse, ndiponso chifukwa chodziwa molondola chinsinsi chopatulika cha Mulungu, chomwe ndi Khristu.+
-