Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 29:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Cholinga cha pangano limeneli n’chakuti, pakati panu pasapezeke mwamuna, mkazi, banja kapena fuko limene mtima wake ukupatuka kusiyana ndi Yehova Mulungu wathu, ndi kupita kukatumikira milungu ya mitundu inayo,+ kuti pakati panu pasapezeke muzu wotulutsa chomera chakupha ndi chitsamba chowawa.+

  • Yohane 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Chakudya chamadzulo chili mkati, Mdyerekezi anali ataika kale maganizo ofuna kupereka Yesu+ mumtima mwa Yudasi Isikariyoti,+ mwana wa Simoni.

  • Machitidwe 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti ndaona kuti ndiwe ndulu yaululu+ ndipo mwa iwe mwadzaza kusalungama.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena