Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 9:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho Yehova wa makamu, Mulungu wa Isiraeli, wanena kuti, ‘Ine ndidzadyetsa anthu amenewa chitsamba chowawa,+ ndipo ndidzawamwetsa madzi apoizoni.+

  • Hoseya 10:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Iwo amalankhula mawu opanda pake, amachita malumbiro abodza,+ amachita mapangano+ ndipo kusalungama kwafalikira ngati zomera zakupha m’mizere ya m’munda.+

  • Amosi 6:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 “‘Kodi mahatchi angathamange pathanthwe, kapena kodi munthu angalime pathanthwe ndi ng’ombe? Anthu inu mwakana chilungamo,+ choncho mwachititsa moyo wa anthu kukhala wowawa.

  • Machitidwe 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pakuti ndaona kuti ndiwe ndulu yaululu+ ndipo mwa iwe mwadzaza kusalungama.”+

  • Aheberi 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pochita zimenezo, muonetsetse kuti wina asalandidwe kukoma mtima kwakukulu kwa Mulungu,+ komanso kuti pakati panu pasatuluke muzu wapoizoni+ woyambitsa mavuto, ndi kuti ambiri asaipitsidwe nawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena