Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 25:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Tsopano Abulahamu anatenganso mkazi wina, dzina lake Ketura. 2 Patapita nthawi, mkaziyo anamuberekera Zimirani, Yokesani, Medani, Midiyani,+ Isibaki ndi Shuwa.+

  • Ekisodo 2:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Farao anamva za nkhaniyi ndipo ankafuna kupha Mose. Koma Mose anathawa Farao nʼkupita kukakhala kudziko la Midiyani.+ Atafika kumeneko, anakhala pafupi ndi chitsime.

  • Numeri 31:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uwabwezere+ Amidiyani chifukwa cha zimene anachitira Aisiraeli.+ Pambuyo pake udzaikidwa mʼmanda ngati mmene anachitira ndi makolo ako.”*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena