Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 25:17-20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mudzapange chivundikiro chagolide woyenga bwino, masentimita 110 mulitali ndi masentimita 70 mulifupi.+ 18 Mupangenso akerubi awiri agolide. Akhale osula ndipo muwaike kumapeto onse awiri a chivundikirocho.+ 19 Kerubi mmodzi akhale kumbali imodzi ya chivundikirocho ndipo kerubi wina akhale kumbali inayo. 20 Akerubiwo atambasule mapiko awo nʼkuwakweza mʼmwamba ndipo aphimbe chivundikirocho ndi mapiko awo.+ Iwo akhale moyangʼanizana, koma nkhope zawo ziweramire pachivundikiro.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena