Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 38:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mwamuna aliyense amene anawerengedwa, kuyambira wa zaka 20 kupita mʼtsogolo,+ anapereka hafu ya sekeli potengera muyezo wa sekeli lakumalo oyera.* Anthu onse amene anawerengedwa analipo 603,550.+

  • Numeri 1:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Iweyo ndi Aroni muwalembe mʼkaundula mogwirizana ndi magulu awo.* Uwerenge onse kuyambira azaka 20 kupita mʼtsogolo,+ amene ali oyenera kupita kunkhondo mu Isiraeli.

  • Numeri 26:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Mliri uja utatha,+ Yehova anauza Mose ndi Eleazara mwana wa wansembe Aroni kuti: 2 “Muwerenge amuna onse oyenera kupita kunkhondo pakati pa gulu lonse la Aisiraeli. Muwerenge kuyambira azaka 20 kupita mʼtsogolo, potengera nyumba za makolo awo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena