Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 16:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma mbuzi imene maere asonyeza kuti ndi yotenga machimo a anthu, aziibweretsa yamoyo nʼkuiimika pamaso pa Yehova kuti machimo a anthu aphimbidwe. Akatero aziitumiza mʼchipululu monga mbuzi yotenga machimo a anthu.+

  • Salimo 103:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mofanana ndi mmene kotulukira dzuwa kwatalikirana ndi kolowera dzuwa,

      Mulungu waikanso zolakwa zathu kutali ndi ife.+

  • Aheberi 13:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho nayenso Yesu anakavutikira kunja kwa geti la mzinda+ kuti ayeretse anthu ndi magazi ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena