Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 28:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kumayambiriro kwa mwezi uliwonse,* muzipereka nsembe yopsereza kwa Yehova. Muzipereka ngʼombe ziwiri zazingʼono zamphongo, nkhosa imodzi yamphongo ndi ana a nkhosa 7 amphongo opanda chilema. Mwana wa nkhosa aliyense azikhala wachaka chimodzi.+

  • Numeri 28:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Pa nyama iliyonse yoperekedwa nsembe, muziperekanso nsembe yachakumwa. Ngʼombe yamphongo muziipereka limodzi ndi vinyo+ wokwana hafu ya muyezo wa hini. Nkhosa yamphongo+ muziipereka limodzi ndi vinyo wokwana gawo limodzi mwa magawo atatu a muyezo wa hini. Ndipo mwana wa nkhosa wamphongo muzimupereka limodzi ndi vinyo wokwana gawo limodzi mwa magawo 4 a muyezo wa hini.+ Zinthu zimenezi muzizipereka monga nsembe yopsereza ya mwezi ndi mwezi ndipo muzizipereka mwezi uliwonse pa chaka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena