Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 22:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Balamu anayankha Mulungu woonayo kuti: “Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu ndi amene watumiza anthuwa kuti adzandiuze kuti, 11 ‘Taonani! Anthu amene achokera ku Iguputo aja adzaza dziko lonse lapansi kumene munthu angayangʼane. Tsopano bwerani, mudzatemberere anthuwa.+ Mwina ndingathe kumenyana nawo nʼkuwathamangitsa.’”

  • Numeri 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kenako Balaki anauza Balamu kuti: “Nʼchifukwa chiyani mwandichitira zimenezi? Ndakubweretsani kuno kuti mudzatemberere adani anga, koma inu mwawadalitsa.”+

  • Nehemiya 13:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pa tsiku limenelo buku la Mose linawerengedwa anthu onse akumva.+ Iwo anapeza kuti mʼbukumo analembamo kuti mbadwa iliyonse ya Amoni ndi ya Mowabu+ isamaloledwe kukhala mʼgulu la anthu a Mulungu woona,+ 2 chifukwa iwowa sanapatse Aisiraeli chakudya ndi madzi. Mʼmalomwake, analemba ganyu Balamu kuti awatemberere.+ Koma Mulungu wathu anasintha temberero limenelo kukhala dalitso.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena