Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 21:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Aliyense amene wamenya munthu mpaka munthuyo kufa ayenera kuphedwa.+ 13 Koma ngati sanamuphe mwadala ndipo Mulungu woona walola kuti zichitike, ndidzakukonzerani malo amene angathawireko.+

  • Numeri 35:14, 15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Mupereke mizinda itatu tsidya lino la Yorodano,+ ndiponso mukapereke mizinda itatu tsidya linalo, mʼdziko la Kanani.+ Imeneyi ikakhala mizinda yothawirako. 15 Mizinda 6 imeneyi ikakhale kothawirako Aisiraeli, mlendo+ komanso munthu aliyense amene akukhala pakati pawo, aliyense amene wapha munthu mwangozi.+

  • Deuteronomo 4:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Pa nthawi imeneyo, Mose anapatula mizinda itatu mbali yakumʼmawa kwa Yorodano.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena