Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Aliyense wopha munthu, nayenso adzaphedwa ndi munthu,*+ chifukwa Mulungu anapanga munthu mʼchifaniziro chake.+

  • Oweruza 9:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Atatero anapita kunyumba kwa bambo ake ku Ofira+ nʼkupha abale ake,+ ana aamuna 70 a Yerubaala, ndipo anawaphera pamwala umodzi. Amene anapulumuka anali Yotamu yekha, mwana wamngʼono mwa ana aamuna a Yerubaala, chifukwa anabisala.

  • Oweruza 9:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Zimenezi zinachitika kuti anthu amene anali ndi mlandu wa magazi abwezeredwe nkhanza zimene anachitira ana aamuna 70 a Yerubaala. Zinachitikanso kuti Abimeleki alangidwe chifukwa chopha azichimwene ake+ ndiponso kuti atsogoleri a ku Sekemu alangidwe chifukwa chothandiza Abimeleki kuti aphe azichimwene akewo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena