Deuteronomo 18:9, 10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Mukakalowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, musakaphunzire kuchita zinthu zonyansa zimene anthu a mitundu yakumeneko akuchita.+ 10 Pakati panu pasapezeke munthu wowotcha mwana wake pamoto,*+ wolosera,+ aliyense wochita zamatsenga,+ aliyense woombeza,+ wanyanga,+ Yesaya 2:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Inu mwasiya anthu anu, nyumba ya Yakobo,+Chifukwa iwo ayamba kutsatira miyambo yambiri ya Kumʼmawa.Akuchita zamatsenga+ ngati AfilisitiNdiponso ali ndi ana ambiri a alendo.
9 Mukakalowa mʼdziko limene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, musakaphunzire kuchita zinthu zonyansa zimene anthu a mitundu yakumeneko akuchita.+ 10 Pakati panu pasapezeke munthu wowotcha mwana wake pamoto,*+ wolosera,+ aliyense wochita zamatsenga,+ aliyense woombeza,+ wanyanga,+
6 Inu mwasiya anthu anu, nyumba ya Yakobo,+Chifukwa iwo ayamba kutsatira miyambo yambiri ya Kumʼmawa.Akuchita zamatsenga+ ngati AfilisitiNdiponso ali ndi ana ambiri a alendo.