Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 16:41, 42
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Iwowa anali limodzi ndi Hemani ndi Yedutuni+ ndiponso amuna onse amene anawasankha mochita kuwatchula mayina kuti azithokoza Yehova,+ chifukwa “chikondi chake chokhulupirika chidzakhalapo mpaka kalekale.”+ 42 Hemani+ ndi Yedutuni anawasiya kuti aziimba malipenga, zinganga ndi zipangizo zina zimene ankagwiritsa ntchito potamanda Mulungu woona* ndipo ana a Yedutuni+ anali alonda apageti.

  • 2 Mbiri 35:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Oimba, ana a Asafu,+ anali pa ntchito yawo mogwirizana ndi lamulo la Davide,+ la Asafu,+ la Hemani ndi la Yedutuni+ yemwe anali wamasomphenya wa mfumu. Alonda apageti anali pamageti osiyanasiyana.+ Iwo sankafunika kusiya ntchito yawo chifukwa Alevi abale awo anawakonzera nyama yawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena