Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezara 10:10, 11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kenako wansembe Ezara anaimirira nʼkuuza anthuwo kuti: “Inu mwachita zosakhulupirika chifukwa mwatenga akazi achilendo+ ndipo mwawonjezera machimo a Isiraeli. 11 Choncho vomerezani machimo anu kwa Yehova Mulungu wa makolo anu ndipo chitani zomusangalatsa. Musiyane ndi anthu a mitundu ina ndiponso akazi achilendowa.”+

  • Nehemiya 9:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pa tsiku la 24 la mwezi umenewu Aisiraeli anasonkhana pamodzi ndipo anasala kudya atavala ziguduli komanso atadzithira dothi kumutu.+ 2 Aisiraeli anadzipatula kwa anthu onse omwe sanali Aisiraeli+ ndipo anaimirira nʼkuyamba kuulula machimo awo komanso zolakwa za makolo awo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena