-
Salimo 75:8Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
Ndithudi, iye adzakhuthula vinyo yense
Ndipo anthu onse oipa padziko lapansi adzamwa mpaka kugugudiza nsenga zake.”+
-
-
Yeremiya 25:15Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
15 Yehova Mulungu wa Isiraeli anandiuza kuti: “Tenga kapu iyi ya vinyo wa mkwiyo imene ili mʼdzanja langa ndipo ukamwetse mitundu yonse imene ndikukutumizako.
-