Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 7:16, 17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Nyumba yako ndi ufumu wako zidzakhalapobe mpaka kalekale. Mpando wako wachifumu udzakhazikika mpaka kalekale.”’”+

      17 Natani anauza Davide mawu onsewa ndiponso masomphenya onse amene anaona.+

  • Salimo 72:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Dzina lake likhalebe mpaka kalekale,+

      Ndipo lipitirize kutchuka kwa nthawi zonse pamene dzuwa lidzakhalepo.

      Ndipo kudzera mwa iye, anthu apeze madalitso.+

      Mitundu yonse ya anthu imutchule kuti ndi wosangalala.

  • Yesaya 11:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Nthambi+ idzaphuka pachitsa cha Jese,+

      Ndipo mphukira+ yotuluka pamizu yake idzabereka zipatso.

  • Yeremiya 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Taonani! Masiku adzafika,” watero Yehova, “pamene ndidzaike mfumu yolungama pampando wachifumu yochokera mʼbanja lachifumu la Davide.*+ Mfumuyo idzalamulira mʼdzikoli+ ndipo idzachita zinthu mwanzeru, motsatira malamulo komanso mwachilungamo.+

  • Yohane 12:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndiyeno gulu la anthulo linamuyankha kuti: “Ife tinamva mʼChilamulo kuti Khristu adzakhala kosatha.+ Nanga inu mukunena bwanji kuti Mwana wa munthu ayenera kukwezedwa mʼmwamba?+ Kodi Mwana wa munthu ameneyo ndi ndani?”

  • Chivumbulutso 22:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ‘Ine Yesu, ndinatumiza mngelo wanga kuti adzachitire umboni zinthu zimenezi kwa iwe kuti zithandize mipingo. Ine ndine muzu komanso mbadwa ya Davide.+ Ndinenso nthanda yowala kwambiri.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena