Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 60:9-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ndi ndani amene adzandibweretse kumzinda wozunguliridwa ndi adani?*

      Ndi ndani amene adzanditsogolere mpaka kukafika ku Edomu?+

      10 Kodi si inu Mulungu amene munatikana,

      Mulungu wathu, amene simukutsogoleranso magulu athu ankhondo?+

      11 Tithandizeni pamene tikukumana ndi mavuto,

      Chifukwa chipulumutso chochokera kwa munthu nʼchopanda pake.+

      12 Mulungu adzatipatsa mphamvu,+

      Ndipo adzapondaponda adani athu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena