Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 8:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Davide anakhazikitsa midzi ya asilikali ku Edomu. Mu Edomu monse anaikamo midzi ya asilikali, moti Aedomu anakhala antchito a Davide+ ndipo Yehova ankathandiza Davide kuti apambane kulikonse kumene wapita.+

  • Salimo 108:10-13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ndi ndani amene adzandibweretse kumzinda wokhala ndi mpanda wolimba kwambiri?

      Ndi ndani amene adzanditsogolere mpaka kukafika ku Edomu?+

      11 Kodi si inu Mulungu amene munatikana,

      Mulungu wathu, amene simukutsogoleranso magulu athu ankhondo?+

      12 Tithandizeni pamene tikukumana ndi mavuto,+

      Chifukwa chipulumutso chochokera kwa munthu nʼchopanda pake.+

      13 Mulungu adzatipatsa mphamvu,+

      Ndipo adzapondaponda adani athu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena