Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Koma amakonda kwambiri chilamulo cha Yehova,+

      Ndipo amawerenga ndi kuganizira mozama* chilamulocho masana ndi usiku.+

       3 Iye adzakhala ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa ngalande za madzi,

      Umene umabereka zipatso mʼnyengo yake,

      Umenenso masamba ake safota.

      Ndipo zonse zimene amachita zimamuyendera bwino.+

  • Miyambo 3:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Mwana wanga, usaiwale zimene ndimakuphunzitsa,*

      Ndipo mtima wako uzisunga malamulo anga.

       2 Ukamachita zimenezi, udzakhala ndi masiku ochuluka

      Komanso moyo wazaka zambiri ndi mtendere.+

  • Yesaya 32:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Zotsatira za chilungamo chenicheni zidzakhala mtendere,+

      Ndipo chilungamo chenicheni chidzabweretsa bata komanso chitetezo chosatha.+

  • Yesaya 48:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Zingakhale bwino kwambiri mutamvera malamulo anga!+

      Mukatero mtendere wanu udzakhala ngati mtsinje+

      Ndipo chilungamo chanu chidzakhala ngati mafunde a mʼnyanja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena