Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 29:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Yehova adzapatsa anthu ake mphamvu.+

      Yehova adzadalitsa anthu ake powapatsa mtendere.+

  • Yesaya 40:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Kwezani maso anu kumwamba ndipo muone.

      Kodi ndi ndani amene analenga zinthu zimenezi?+

      Ndi amene akutsogolera gulu lonse la nyenyezi ndipo zonse amaziwerenga.

      Iliyonse amaiitana poitchula dzina lake.+

      Chifukwa cha kuchuluka kwa mphamvu zake zoopsa ndiponso chifukwa chakuti ali ndi mphamvu zambiri zochitira zinthu,+

      Palibe iliyonse imene imasowa.

  • Afilipi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pa zinthu zonse, ndimapeza mphamvu kuchokera kwa Mulungu amene amandipatsa mphamvu zimene ndikufunikira.+

  • Aheberi 11:33, 34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Chifukwa cha chikhulupiriro, anthu amenewa anagonjetsa maufumu pankhondo,+ anachita chilungamo, analonjezedwa zinthu zina+ ndiponso anatseka mikango pakamwa.+ 34 Sanapse ndi moto,+ sanaphedwe ndi lupanga,+ anali ofooka koma anapatsidwa mphamvu,+ anamenya nkhondo mwamphamvu+ ndiponso anathamangitsa magulu ankhondo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena