Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:49, 50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Yehova adzatumiza mtundu wakutali+ kuchokera kumalekezero adziko lapansi kuti udzakuukireni. Mtunduwo udzakuukirani mofulumira kwambiri ngati mmene chiwombankhanga chimagwirira nyama.+ Mtundu umenewo chilankhulo chake simudzachimva,+ 50 mtundu wooneka moopsa umene sudzamvera chisoni munthu wachikulire kapena kuchitira chifundo mnyamata.+

  • Yeremiya 5:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “Ndikukubweretserani mtundu wa anthu kuchokera kutali, inu a mʼnyumba ya Isiraeli,”+ akutero Yehova.

      “Umenewu ndi mtundu umene wakhalapo kwa nthawi yaitali,

      Ndi mtundu wakale kwambiri,

      Mtundu umene chilankhulo chake simukuchidziwa,

      Ndipo simungamve zimene amalankhula.+

  • 1 Akorinto 14:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 MʼChilamulo muli mawu akuti: “‘Anthu awa ndidzawalankhula ndi malilime a anthu achilendo, ndipo ndidzawalankhula ndi milomo ya anthu achilendo, koma iwo adzakana kundimvera,’ watero Yehova.”*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena