Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 15:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mtima wanga ukulirira Mowabu.

      Anthu ake athawira kutali, ku Zowari+ ndi ku Egilati-selisiya.+

      Iwo akulira pamene akukwera mtunda wa Luhiti.

      Panjira yopita ku Horonaimu, iwo akulira kwambiri chifukwa cha tsokalo.+

  • Yeremiya 48:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 “‘Kulira kochokera ku Hesiboni+ kukumveka ku Eleyale.+

      Kulira kwawo kukumveka mpaka ku Yahazi,+

      Kukumveka kuchokera ku Zowari kukafika ku Horonaimu+ ndi ku Egilati-selisiya.

      Ngakhale madzi a ku Nimurimu adzauma.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena