Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 3:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako iye anapanga chipinda cha Malo Oyera Koposa.+ Mulitali mwake chinali mikono 20 mofanana ndi mulifupi mwa nyumbayo ndipo mulifupi mwake chinali mikono 20. Anachikuta ndi golide wabwino wokwana matalente* 600.+

  • Ezekieli 41:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Kenako anayeza chipinda chimene chinayangʼanizana ndi malo oyera, ndipo anapeza kuti chinali mikono 20 mulitali ndi mikono 20 mulifupi.+ Ndiyeno anandiuza kuti: “Amenewa ndi Malo Oyera Koposa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena