Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu mukabwera kudzaonekera pamaso panga,+

      Kodi ndi ndani amene amakuuzani kuti muchite zimenezi,

      Ndi ndani amene amakuuzani kuti muzipondaponda mabwalo a panyumba panga?+

  • Yesaya 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndipo mukatambasula manja anu,

      Ndimakubisirani maso anga.+

      Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+

      Ine sindimvetsera.+

      Manja anu adzaza magazi.+

  • Ezekieli 14:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Iwe mwana wa munthu, amuna awa atsimikiza mumtima mwawo kuti azitsatira mafano awo onyansa,* ndipo aika chinthu chopunthwitsa chimene chimachititsa kuti anthu azichimwa. Kodi ndiwayankhe iwo akamandifunsa?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena