Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 37:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Ndiyeno mngelo wa Yehova anapita kumsasa wa Asuri nʼkukapha asilikali 185,000. Anthu podzuka mʼmawa, anangoona kuti onse ndi mitembo yokhayokha.+

  • Zekariya 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndidzadutsa panyanja, nyanjayo nditaigwetsera tsoka.

      Ndidzamenya mafunde a nyanjayo,+

      Ndipo madzi onse a mtsinje wa Nailo adzauma.

      Kunyada kwa Asuri kudzathetsedwa,

      Ndipo ndodo yachifumu ya Iguputo idzachoka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena