Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 22:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kudzera mwa mbadwa* yako,+ mitundu yonse yapadziko lapansi idzapeza madalitso chifukwa chakuti wamvera mawu anga.’”+

  • Yesaya 19:24, 25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Pa tsiku limenelo, anthu a ku Isiraeli adzakhala gulu lachitatu, ataphatikizana ndi Aiguputo komanso Asuri,+ amenewa adzakhala madalitso padziko lapansi, 25 chifukwa Yehova wa magulu ankhondo akumwamba adzakhala atawadalitsa nʼkuwauza kuti: “Adalitsike Aiguputo anthu anga, Asuri ntchito ya manja anga komanso Aisiraeli omwe ndi cholowa changa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena