Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 49:19, 20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Ngakhale kuti malo ako anawonongedwa komanso kusakazidwa ndipo dziko lako linali mabwinja,+

      Tsopano anthu amene adzakhale mmenemo malo adzawachepera moti adzakhala mopanikizana,+

      Ndipo anthu amene anakumeza+ adzakhala kutali.+

      20 Ana ako amene unabereka ana ena onse atamwalira, adzakuuza kuti,

      ‘Malowa atichepera.

      Tipezereni malo oti tizikhalamo.’+

  • Yesaya 54:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 “Fuula mosangalala iwe mkazi amene sunaberekepo mwana.+

      Iwe amene sunamvepo zowawa za pobereka,+ sangalala ndipo ufuule mosangalala.+

      Chifukwa ana a mkazi wosiyidwa ndi ambiri

      Kuposa ana a mkazi yemwe ali ndi mwamuna,”*+ akutero Yehova.

       2 “Kulitsa tenti yako.+

      Tambasula nsalu za chihema chako chachikulu.

      Usaumire pochita zimenezi. Talikitsa zingwe za tenti yako

      Ndipo ulimbitse zikhomo zake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena