Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 8:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Saulo anayamba kuzunza mpingo mwankhanza. Ankalowa mʼnyumba iliyonse nʼkumakokera panja amuna ndi akazi omwe, ndipo ankawapititsa kundende.+

  • Agalatiya 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Munamva ndithu zimene ndinkachita ndili mʼChiyuda,+ kuti ndinkazunza kwambiri mpingo wa Mulungu ndipo ndinapitiriza kuuwononga.+

  • Agalatiya 1:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iwo ankangomva kuti: “Munthu amene kale ankatizunza uja+ komanso kuwononga mipingo* tsopano akulengeza uthenga wabwino.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena