Machitidwe 18:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Popeza ntchito yawo inali imodzi, anakhala kunyumba kwawoko. Iwo ankagwirira ntchito limodzi,+ chifukwa onse anali opanga matenti. 1 Akorinto 4:11, 12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Mpaka pano tikadali anjala,+ aludzu+ ndiponso ausiwa. Tikumenyedwabe,+ tikusowabe pokhala 12 ndipo tikugwirabe ntchito mwakhama ndi manja athu.+ Akamatinenera zachipongwe, timadalitsa+ ndipo akamatizunza, timapirira moleza mtima.+ 1 Atesalonika 2:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Ndithudi abale, mukukumbukira kuti tinayesetsa kugwira ntchito mwakhama ndi mphamvu zathu zonse. Tinkagwira ntchito usiku ndi masana kuti aliyense wa inu asatilipirire kanthu kalikonse pofuna kutithandiza,+ pamene tinkalalikira uthenga wabwino wa Mulungu kwa inu.
3 Popeza ntchito yawo inali imodzi, anakhala kunyumba kwawoko. Iwo ankagwirira ntchito limodzi,+ chifukwa onse anali opanga matenti.
11 Mpaka pano tikadali anjala,+ aludzu+ ndiponso ausiwa. Tikumenyedwabe,+ tikusowabe pokhala 12 ndipo tikugwirabe ntchito mwakhama ndi manja athu.+ Akamatinenera zachipongwe, timadalitsa+ ndipo akamatizunza, timapirira moleza mtima.+
9 Ndithudi abale, mukukumbukira kuti tinayesetsa kugwira ntchito mwakhama ndi mphamvu zathu zonse. Tinkagwira ntchito usiku ndi masana kuti aliyense wa inu asatilipirire kanthu kalikonse pofuna kutithandiza,+ pamene tinkalalikira uthenga wabwino wa Mulungu kwa inu.