Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Machitidwe 9:3-5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ali pa ulendo wakewo, atatsala pangʼono kufika ku Damasiko, mwadzidzidzi anangoona kuwala kochokera kumwamba kutamuzungulira.+ 4 Zitatero anagwa pansi ndipo anamva mawu akuti: “Saulo, Saulo, nʼchifukwa chiyani ukundizunza?” 5 Iye anafunsa kuti: “Mbuyanga, ndinu ndani kodi?” Anamuyankha kuti: “Ndine Yesu,+ amene ukumuzunza.+

  • 1 Akorinto 15:7, 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Atatero anaonekera kwa Yakobo,+ kenako kwa atumwi onse.+ 8 Koma pomaliza anaonekera kwa ine,+ ngati khanda lobadwa masiku osakwana.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena