Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 21:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Taonani zimene zikubwera:

      Kukubwera amuna amene akwera galeta lankhondo limene likukokedwa ndi mahatchi awiri.”+

      Kenako iye analankhula kuti:

      “Wagwa! Babulo wagwa!+

      Zifaniziro zonse zogoba za milungu yake zaphwanyidwa ndipo zili pansi.”+

  • Chivumbulutso 18:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndiyeno mngelo wamphamvu ananyamula mwala wooneka ngati mphero yaikulu nʼkuuponya mʼnyanja, ndipo anati: “Mzinda waukulu wa Babulo udzaponyedwa pansi mofulumira ndi mwamphamvu chonchi, ndipo sudzapezekanso.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena