Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • g 10/12 tsamba 2
  • Kodi Mungatani Kuti Zizikuyenderani ku Sukulu?

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kodi Mungatani Kuti Zizikuyenderani ku Sukulu?
  • Galamukani!—2012
  • Nkhani Yofanana
  • Zimene Mungachite Ngati Simukusangalalanso ndi Sukulu
    Zimene Achinyamata Amafunsa
  • Sukulu Yopambana Yapadziko Lonse
    Galamukani!—1996
  • Kodi Ndisiye Sukulu?
    Galamukani!—2010
  • Bwanji Ndingosiya Sukulu?
    Mayankho a Zimene Achinyamata Amafunsa, Buku Loyamba
Onani Zambiri
Galamukani!—2012
g 10/12 tsamba 2

Zimene Mungachite Kuti Zizikuyenderani ku Sukulu

Pa mawu ali m’munsiwa, kodi ndi mawu ati amene akufotokoza mmene inuyo mumaonera sukulu?

  • Yotopetsa kapena yosangalatsa?

  • Yovuta kapena yopindulitsa?

  • Yosafunika kapena yothandiza?

Ngati inuyo mumaona kuti sukulu ndi yosasangalatsa, kodi mungatani kuti muyambe kuikonda? Ngati mumaikonda, kodi mungatani kuti mupindule nayo kwambiri? Patsamba 3 mpaka 7, pali mfundo zisanu za m’Baibulo, zomwe zingakuthandizeni kuti zinthu zizikuyenderani bwino ku sukulu.

Mfundo zambiri zomwe zili mu nkhani zimenezi zingathandize ana omwe amapita ku sukulu yaboma kapena yapulaiveti.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena