Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • le tsamba 16-17
  • Mmene Tikupulumutsidwira ku Uchimo ndi Imfa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mmene Tikupulumutsidwira ku Uchimo ndi Imfa
  • Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Yesu Amapulumutsa Motani?
    Nsanja ya Olonda—2001
  • Nchifukwa Chiyani Yesu Anavutika Mpaka Kufa?
    Nsanja ya Olonda Yolengeza Ufumu wa Yehova (Yogawira)—2016
  • N’chifukwa chiyani Yesu Anafa?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
  • N’chifukwa Chiyani Anthu Amafa?
    Kuyankha Mafunso a M’Baibulo
Onani Zambiri
Sangalalani Ndi Moyo pa Dziko Lapansi Kosatha!
le tsamba 16-17

Mmene Tikupulumutsidwira ku Uchimo ndi Imfa

35 Kodi mukukumbukira kuti Adamu, mwamuna woyambirira, anachimwa? Iye anataya moyo ndi paradaiso, ndipo tonsefe timafanso, chifukwa chakuti ndife ana ake.—Aroma 5:12; 3:23

36 Tikatha kupezanso moyo wangwiro umenewu, ngati munthu wina wangwiro anapereka moyo wake kaamba ka ife, kapena anatiombola ku imfa.—1 Akorinto 15:45; Aroma 5:19, 21

37 Yesu anali mwana wa Mulungu. Iye anali munthu wangwiro. Iye sanachimwe.—Ahebri 5:9; 7:26

38 Iye anadzilola kuphedwa ndi anthu amene sanakonde Mulungu.—Machitidwe 2:23

Kumeneku kunali kudzipereka yekha nsembe kaamba ka ife.—1 Timoteo 2:6

39 Yesu anaikidwa m’phanga losemedwa kapena manda. Iye anali wakufa kwa masiku atatu. Kenako Mulungu anam’dzutsa.—Machitidwe 2:24

40 Iye anabwerera kumwamba. Iye tsopano angathe kupempha Mulungu kuthandiza awo amene amamvera Mulungu.—Ahebri 9:24; 1 Yohane 2:1, 2

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena