Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 12/15 tsamba 25
  • Kufunafuna kaamba ka Chowonadi Kufupidwa

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Kufunafuna kaamba ka Chowonadi Kufupidwa
  • Nsanja ya Olonda—1987
  • Nkhani Yofanana
  • Carici Coona ndi Maziko Ace
    Coonadi Cimene Cimatsogolera ku Moyo Wamuyaya
  • Ziyembekezo za Mtsogolo Kaamba ka chiProtestanti—Ndi Inu!
    Galamukani!—1988
  • Kodi ma Lutheran AchiGerman ali Mtundu Wowopsyezedwa?
    Galamukani!—1988
  • ‘Yesetsani Kufunafuna Yehova Kuti Mupitirize Kukhala ndi Moyo’
    Utumiki Komanso Moyo Wathu wa Chikhristu—Ndandanda ya Misonkhano—2017
Nsanja ya Olonda—1987
w87 12/15 tsamba 25

Kufunafuna kaamba ka Chowonadi Kufupidwa

MWA kupeza kukhutiritsidwa kochepa monga mlaliki wamba mu tchalitchi cha Chipresbyterian, mwamuna wina anayamba kufunafuna kaamba ka tchalitchi chowona cha Mulungu. Iye anandandalitsa zofunika khumi zomwe iye anadzimva kuti tchalitchi chowona chifunikira kukhala nazo. Iye anali kale ndi kumvetsetsa kolongosoka kwa moto wa helo wosakhala wa m’malemba, kusafa kwa moyo, ndi zina zotero. Iye anachita kufufuzaku kwa zaka 30. Pamene anakumanidwa ndi mmodzi wa Mboni za Yehova, anayamba kufunsa mafunso ake, onga ngati: “Ndani omwe ali kagulu ka nkhosa? Ndani omwe ali a 144,000 ndi nkhosa zina?” Atapeza mayankho okhutiritsa iye anavomereza ku phunziro la Baibulo. Pambuyo pa miyezi itatu iye anati kwa mboniyo: “Chabwino Mbale, tchalitchi chowona cha Mulungu chiri cha Mboni za Yehova.” Iye tsopano ali ndi zaka 71 za kubadwa ndipo wachimwemwe kukhala atapeza tchalitchi chowona pambuyo pa kufunafuna kwa zaka 30!

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena