Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w87 12/15 tsamba 31
  • Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1987

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1987
  • Nsanja ya Olonda—1987
  • Timitu
  • CHIDZIŴITSO PA NYUZI
  • MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA
  • MBIRI YA MOYO WA MUNTHU
  • MBONI ZA YEHOVA
  • MFUNDO ZAZIKULU ZA BAIBULO
  • MOYO NDI UMINISITALA ZA YESU
  • MOYO WACHIKRISTU NDI MIKHALIDWE
  • NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA
  • NKHANI ZOSIYANASIYANA
  • RIPOTI LA OLENGEZA UFUMU
  • YEHOVA
Nsanja ya Olonda—1987
w87 12/15 tsamba 31

Chosonyezera Nkhani za mu Nsanja ya Olonda za 1987

Chosonyeza deti la kope m’limene nkhaniyo ikupezeka

CHIDZIŴITSO PA NYUZI

1/15, 6/15, 10/15

MAFUNSO OCHOKERA KWA OŴERENGA

2 Akorinto 12:8, 9, 11/15

“Bukhu la moyo la Mulungu,” 9/1

Cholakwa cha Mose, 10/15

“Dziko latsopano”? 5/1

Kukwatiranso mnzanu wa mu ukwati pa chiwukiriro? 6/1

Kulira kwa Yesu ‘mwandisiiranji?’ 6/15

Kupenda thupi, 4/1

Malaki 2:15, 9/15

Miyambo 30:4, 7/15

Nchifukwa ninji mtembenuki wa Afarisi anasandutsidwa mwana wa Gehena? 10/1

Ngamira kapena chingwe kupyola diso la singano? 12/1

“Zinthu zovumbulutsidwa” (Deut. 29:29), 5/15

MBIRI YA MOYO WA MUNTHU

‘Chikho Changa Chasefukira’ (T. Gott), 6/1

Kukhala Moyandikira ku gulu la Yehova (J. Barr), 7/1

Kuyang’ana M’mbuyo Kuposa Zaka 93 za Kukhala ndi Moyo (F. W. Franz), 5/1

Mbadwo Wanga​—Wapadera ndi wa Mwaŵi Wapamwamba (M. Sargent), 8/1

Ndawona Kuti Yehova Ali Wabwino (L. Johnson), 10/1

Yehova Akutichinjiriza (E. Kattner), 4/1

MBONI ZA YEHOVA

“Achangu Kaamba ka Ntchito Zabwino” mu Kenya, 4/15

Chikondwerero Pakati pa Anthu a Mulungu, 1/1

Chiwonjezeko Chabwino “Kuseri kwa Mapiri” (Haiti), 11/1

Chiwonjezeko mu Gibraltar, 10/15

“Chokumana Nacho Cholemera,” 4/1

Chokwaniritsa Chozizwitsa cha Costa Rica, 9/1

Dziko la Zinenero 700 (Papua New Guinea), 9/15

Kuitana kwa Zisumbu za Micronesia, 11/15

Kukhulupirika kwa Chikristu mu New Caledonia, 8/15

Kumaliza Maphunziro kwa Gileadi, 6/1, 12/1

M’munda wa Umishonale, 1/15

Mphatso Yapadera ya Ana, 8/1

Msonkhano wa Chigawo wa “Khulupirirani Yehova,” 2/1

Sukulu Yatsopano Yodzatsegulidwa! 6/1

Ufulu wa Chipembedzo Usungidwa mu India, 11/1

Yehova Amanga Nyumba (South Africa), 12/15

MFUNDO ZAZIKULU ZA BAIBULO

Masalmo 107-150, 3/15

Miyambo, 5/15

Mlaliki, 9/15

Nyimbo ya Solomo, 11/15

MOYO NDI UMINISITALA ZA YESU

(Nkhani zowoneka m’kope lirilonse.)

MOYO WACHIKRISTU NDI MIKHALIDWE

Akazi M’malo a Ntchito, 3/15

Anthu Achimwemwe​—Nchifukwa Ninji? 3/15

Chikhulupiriro Chingasunthe Mapiri! 7/15

Chikristu Chowona Chimatulutsa Akristu Opanda Maziko? 7/15

Kodi Kupatsa Kwanu Kuli Nsembe? 12/1

Kodi Miyambo Imalamulira Moyo Wanu? 2/1

Kodi Mudzamamatira ku Chowonadi? 3/15

Kodi Nthaŵi Zonse Mumagwira Nsonga? 4/1

Kuchita ndi Mkwiyo, 7/1

Kusamalira Banja​—Kodi Kumafutukuka Kufika ku Utali Wotani? 6/15

Kusamalira Okalamba, 6/1

Kuthandiza Mwana Kuti Akule mu Nzeru ya Umulungu, 12/15

Mankhwala a Mwambo mu Africa, 4/15

Mmene Mungapangire Mabwenzi Owona, 9/15

‘Mulungu Adzatsiriza Kuphunzitsidwa Kwanu,’ 6/15

“Nthaŵi Yolankhula​—Liti? 9/1

Phindu la Kuimba M’kulambira Kowona, 12/1

Thandizo M’kupanga Zosankha za Nzeru, 5/15

Zakumwa Zoledzeretsa, 8/1

NKHANI ZAZIKULU ZOPHUNZIRIDWA

Achichepere​—Kodi Mudzachitanji ndi Moyo Wanu? 8/15

Achichepere​—Kodi Mukupita Patsogolo Mwauzimu? 8/15

Achimwemwe ali Awo Amene Amagwiritsira Ntchito Mphamvu Moyenera, 3/1

Ana Amene Amakondweretsa Mtima wa Yehova, 12/15

Ana​—Musanyengedwe, 12/15

Chaka Choliza Lipenga cha Akristu Chifika pa Chimake mu Zaka Chikwi, 1/1

Chaka Choliza Lipenga cha Yehova​—Nthaŵi Yathu ya Kusangalala, 1/1

Chenjerani ndi Kugwiritsira Ntchito Molakwika Mphamvu, 3/1

Chilango Chimabala Chipatso cha Mtendere, 10/1

Chisungiko cha Dziko Lonse Pansi pa “Kalonga wa Mtendere,” 4/1

Dziko Lapansi Silinayenera Iwo, 1/15

“Ine Ndiimabe Pamwamba pa Nsanja,” 3/1

Khulupirirani Yehova​—Osati mu “Chiwembu!” 9/1

Kodi Mapemphero Anu Ali Atanthauzo Motani? 7/15

Kodi Mudzanena Kuti, “Ndine Pano! Munditumize Ine”? 10/15

Kodi Mukukhalabe Osadetsedwa M’njira Iriyonse? 11/1

Kodi Muli Okhutiritsidwa ndi Makonzedwe Auzimu a Yehova? 10/1

Kristu Mokangalika Akutsogolera Mpingo Wake, 8/1

Kubadwa kwa Mwana Kwakukulu Koposa kwa Padziko Lapansi Kutsogolera ku Chisungiko cha Dziko Lonse, 4/1

Kugwirizana ndi Osunga Umphumphu a Yehova, 1/1

Kukhala Ogalamuka Molimbana ndi “Mtendere ndi Chisungiko” Monga Kwaganiziridwa ndi Mitundu, 9/1

Kulemekeza Mulungu wa Chiyembekezo, 12/15

Kulungamitsa Zinthu Pakati pa Mulungu ndi Inu, 10/15

Kumachita Mmene Tingathere Kulalikira Mbiri Yabwino, 2/1

Kumamvera Yehova Pamene Mapeto Akuyandikira, 5/15

Kumayang’anitsitsa pa Zikondwerero za Okalamba, 6/1

‘Kumayenda M’njira ya Chowonadi,’ 3/1

Kupanga Zinthu Zonse Kukhala Zatsopano, 3/1

Kupeza Mtendere ndi Mulungu mwa Kudzipereka ndi Ubatizo, 4/15

Kuphunzira Kupembedza Mulungu Kulinga kwa Makolo Okalamba, 6/1

Kupulumutsa Moyo M’nthawi ya Njala, 5/1

Kupuma “Mpweya” wa Dziko Lino Kuli Kwakupha! 9/15

Kusonyeza Chiyamikiro Kaamba ka Zisonyezero Ziŵiri Zazikulu Kwambiri za Chikondi, 12/15

Kuwopa Mulungu​—Kodi Kungakupindulitseni? 12/1

Kuyesedwa ndi Kusefedwa M’nthaŵi Zamakono, 6/15

Lankhulani Ponena za Ulemelero wa Ufumu wa Mulungu, 10/15

Madalitso Aumulungu kwa “Awo Okhala ndi Chidziŵitso,” 7/1

Mapemphero Amafunikira Zintchito, 7/15

Mikayeli Kalonga Wamkulu Aimirira, 7/1

Mmene Mungakumanire ndi Mtendere Waumulungu Mokwanira Kwambiri, 3/15

Mtambo Waukulu Wotere wa Mboni! 1/15

Mtendere Potsirizira!​—Pamene Mulungu Alankhula, 5/15

Mtendere Waumulungu Kaamba ka Awo Ophunzitsidwa ndi Yehova, 3/15

“Muzikhala Oyera Mtima . . . ” 11/1

Njala Yopatsa Imfa mu Nthaŵi ya Mwana Alirenji, 5/1

Nthaŵi ya Kuyesedwa ndi Kusefedwa, 6/15

Onjezerani Mtendere Wanu Mwachidziŵitso Cholongosoka, 4/15

‘Palibe Mtendere kwa Oipa,’ 7/1

Pitirizani Kugonjera ku “Mzimu Womwe Uli Wopatsa Moyo,” 9/15

Pitirizani Kukhala ndi Moyo Monga Ana a Mulungu, 2/1

Pitirizani Kuyenda M’kuwunika kwa Umulungu, 1/15

Sungani Kuwopa Kwanu Yehova, 12/1

Sonyezani Chikondi ndi Chikhulupiriro Nthaŵi Zonse, 2/1

Sonyezani Kufunitsitsa ku Kulalikira Mbiri Yabwino, 2/1

Umbeta​—Njira Yopatsa Mphoto ya Moyo, 11/15

Utsogoleri Wokangalika wa Kristu Lerolino, 8/1

Wosakwatira koma Wokwanira Kaamba ka Utumiki wa Mulungu, 11/15

Yembekeza Yehova, 12/15

Zisonyezero Ziŵiri Zazikulu Kwambiri za Chikondi, 12/15

NKHANI ZOSIYANASIYANA

Anabaptists, 11/15

Angelo​—Amayambukira Moyo Wanu? 12/15

Baibulo la William Tyndale, 7/15

Chifuno cha Ulosi, 5/1

Chipembedzo Chingakhutiritse Zosowa Zathu? 11/15

Chipembedzo Mphamvu ya Makhalidwe Abwino? 10/15

Funde Lalikulu la Chipembedzo​—Chiitano Chomalizira, 11/1

Kodi Chipembedzo Chamakono Chiri Chogwira Ntchito Motani? 10/1

Kodi Miyendo Yake Inali Kuti? 8/15

Kodi Mtanda uli wa Akristu? 8/15

Kuchiritsa kwa Chikhulupiriro​—Kuchokera kwa Mulungu? 12/1

Kuchita Ulauli, 3/1

Kuchokera ku Ukapolo Wopanga Njerwa Kupita ku Ufulu! 11/15

Kukhulupirira Malaulo, 11/1

Kukhulupirira Mizimu​—Kumawonedwa Motani ndi Mulungu? 9/1

Kunyalanyaza Machenjezo ndi Kuyesa Mulungu, 12/15

Kuwopsya kwa Chuma ndi Umphaŵi, 9/15

Lalikirani Ufulu! 1/1

Madzi Akukonzanso Aphulika, 10/1

Maulosi Onse Amachokera kwa Mulungu? 5/1

Mbali Yowongoleredwa ya Akazi, 8/15

Mbiri ya Chipembedzo iri ya Phindu Lirilonse? 9/15

Mumadera Nkhaŵa Ponena za Ana Anu? 12/15

“Utatu Wodalitsidwa”​—Kodi Uli mu Baibulo? 6/15

Uthenga wa Mayanjano, 1/15

RIPOTI LA OLENGEZA UFUMU

(M’kope lirilonse la 1 la mwezi.)

YEHOVA

Kodi Mulungu Ali Munthu Weniweni? 4/1

Kodi Nchiyani Chimene Mulungu Wachita Kaamba ka Inu? 5/15

Nzeru ya Mulungu Kodi Mukuiwona Iyo? 4/15

Wokhalako Wamkulukulu Ali Wapadera, 6/15

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena