Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • w12 8/15 tsamba 1-2
  • Zamkatimu

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Zamkatimu
  • Nsanja ya Olonda—2012
  • Timitu
  • NKHANI ZOPHUNZIRA
  • CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA
  • M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI
Nsanja ya Olonda—2012
w12 8/15 tsamba 1-2

Zamkatimu

August 15, 2012

© 2012 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania. Ulamuliro wonse pa magazini ino ndi wathu.

Magazini Yophunzira

NKHANI ZOPHUNZIRA

SEPTEMBER 24-30, 2012

“Ine Ndili Pamodzi ndi Inu”

TSAMBA 3 • NYIMBO: 65, 2

OCTOBER 1-7, 2012

Muzichita Zinthu Monga Nzika za Ufumu

TSAMBA 11 • NYIMBO: 16, 98

OCTOBER 8-14, 2012

Samalani ndi Misampha ya Mdyerekezi

TSAMBA 20 • NYIMBO: 61, 25

OCTOBER 15-21, 2012

Musasunthike Popewa Misampha ya Satana

TSAMBA 25 • NYIMBO: 32, 83

CHOLINGA CHA NKHANI ZOPHUNZIRA

NKHANI YOPHUNZIRA 1 TSAMBA 3-7

Danieli analosera kuti “nthawi yamapeto,” anthu ambiri adzadziwa “zinthu zambiri zoona.” (Dan. 12:4) Nkhaniyi ikufotokoza za kukwaniritsidwa kwa ulosiwu. Ikufotokozanso umboni wosonyeza kuti Yesu akuthandiza anthu amene akutumikira Yehova Mulungu.

NKHANI YOPHUNZIRA 2 TSAMBA 11-15

Nkhaniyi ikuthandizani kudziwa nzika za Ufumu. Ikufotokoza zimene anthu ayenera kuchita kuti akhale nzika. Ikufotokozanso mmene nzikazo zingasonyezere kuti zimakonda malamulo a Yehova.

NKHANI ZOPHUNZIRA 3, 4 TSAMBA 20-29

Satana amagwiritsa ntchito misampha mochenjera kuti asokoneze chikhulupiriro chathu. Nkhanizi zikufotokoza mmene tingadzitetezere ku misampha isanu. Misamphayo ndi kusalankhula bwino, kuopa anthu ndiponso kufuna kuwasangalatsa, kudziimba mlandu kwambiri, kukonda chuma ndiponso chigololo.

M’MAGAZINI INO MULINSO NKHANI IZI

8 “Mudzapeza Mphoto Chifukwa cha Ntchito Yanu”

16 Palidi Mgwirizano Ndiponso Mapulani Abwino

30 Kodi Mukukumbukira?

31 Kale Lathu

PATSAMBA LOYAMBA: Wofalitsa akulalikira m’busa kudera lotchedwa Bafatá ku Guinea-Bissau

GUINEA-BISSAU

KULI ANTHU

1,515,000

KULI OFALITSA

120

MAPHUNZIRO A BAIBULO

389

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena