Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • km 6/98 tsamba 2
  • Mbiri Yateokrase

Palibe Vidiyo.

Pepani vidiyoyi ikukanika kutsegula.

  • Mbiri Yateokrase
  • Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
  • Nkhani Yofanana
  • Kodi Chuma Chakuthupi Chingatsimikiziritse Kupeza Chimwemwe?
    Galamukani!—1994
Utumiki Wathu wa Ufumu—1998
km 6/98 tsamba 2

Mbiri Yateokrase

◼ Muno m’Malaŵi, ntchito yomanga pamalo a Sosaite ku Lilongwe inayamba Loŵeruka, pa March 21, pamene mpanda unayamba kumangidwa. Ntchito yomanga Beteliyo akuyembekezera kudzaitsiriza m’chaka cha 2000.

◼ Nthambi zingapo za m’zisumbu padziko lonse zinapereka lipoti la ziŵerengero zatsopano zapamwamba za ofalitsa mu January. Nthambi zinazo zinali Dominican Republic, Haiti, Martinique, Mauritius, Philippines, Taiwan, ndi Trinidad.

◼ Chiwonjezeko cha ku Seychelles chinali 18 peresenti kuposa avareji ya chaka chatha, ndipo cha ku St. Maarten chinali 16 peresenti.

◼ Ku Hong Kong ofalitsa anachita avareji ya maola 12.7.

◼ Nyumba ya Ufumu yoyamba yomangidwa masiku oŵerengeka ku Taiwan inamalizidwa mu February.

    Mabuku a Chichewa (1974-2025)
    Tulukani
    Lowani
    • Chichewa
    • Tumizirani Ena
    • Zimene Mumakonda
    • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
    • Zoyenera Kutsatira
    • Nkhani Yosunga Chinsinsi
    • Privacy Settings
    • JW.ORG
    • Lowani
    Tumizirani Ena